Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo mkulu wa ansembe anati, Zitero izi kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo mkulu wa ansembe anati, Zitero izi kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mkulu wa ansembe onse adafunsa Stefano kuti, “Kodi zimenezi nzoona?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Kenaka mkulu wa ansembe anafunsa Stefano kuti, “Kodi zimene akukunenerazi ndi zoona?”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anampenyetsetsa onse akukhala m'bwalo la akulu a milandu, naona nkhope yake ngati nkhope ya mngelo.


Ndipo Stefano anati, Amuna inu, abale, ndi atate, tamverani. Mulungu wa ulemerero anaonekera kwa kholo lathu Abrahamu, pokhala iye mu Mesopotamiya, asanayambe kukhala mu Harani;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa