Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 5:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Petro ananena naye, Undiuze, ngati munagulitsa mundawo pa mtengo wakuti. Ndipo ananena, Inde, wakuti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Petro ananena naye, Undiuze, ngati munagulitsa mundawo pa mtengo wakuti. Ndipo ananena, Inde, wakuti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Petro adamufunsa kuti, “Tandiwuzani, kodi pogulitsa munda wanu, mtengo wake unali ndalama izi?” Maiyo adati, “Inde, mtengo wake unali womwewo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Petro anamufunsa iye kuti, “Tandiwuza, kodi izi ndi ndalama zonse zimene iwe ndi Hananiya munalandira mutagulitsa munda?” Mkaziyo anati, “Inde ndi zimenezo.”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 5:8
2 Mawu Ofanana  

anagulitsa chao, napatula pa mtengo wake, mkazi yemwe anadziwa, natenga chotsala, nachiika pa mapazi a atumwi.


Koma atapita monga maora atatu, ndipo mkazi wake, wosadziwa chidachitikacho, analowa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa