Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 5:7 - Buku Lopatulika

7 Koma atapita monga maora atatu, ndipo mkazi wake, wosadziwa chidachitikacho, analowa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Koma atapita monga maora atatu, ndipo mkazi wake, wosadziwa chidachitikacho, analowa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Patapita ngati maora atatu, mkazi wake adaloŵa, osadziŵa zimene zachitika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Patapita maora atatu mkazi wake analowa, wosadziwa zimene zinachitika.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 5:7
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ananyamuka anyamata, namkulunga, namnyamula, natuluka naye, namuika.


Ndipo Petro ananena naye, Undiuze, ngati munagulitsa mundawo pa mtengo wakuti. Ndipo ananena, Inde, wakuti.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa