Machitidwe a Atumwi 5:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo ananyamuka anyamata, namkulunga, namnyamula, natuluka naye, namuika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo ananyamuka anyamata, namkulunga, namnyamula, natuluka naye, namuika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono achinyamata adabwera namkulunga m'nsalu. Adamnyamula nakamuika m'manda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kenaka anyamata anafika, nakulunga thupi lake, ndipo anamunyamula ndi kukamuyika mʼmanda. Onani mutuwo |