Machitidwe a Atumwi 5:41 - Buku Lopatulika41 Pamenepo ndipo anapita kuchokera kubwalo la akulu a milandu, nakondwera kuti anayesedwa oyenera kunyozedwa chifukwa cha dzinalo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Pamenepo ndipo anapita kuchokera kubwalo la akulu, nakondwera kuti anayesedwa oyenera kunyozedwa chifukwa cha dzinalo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Iwo adachoka kubwaloko ali okondwa kuti Mulungu waŵaŵerengera ngati oyenera kunyozeka chifukwa cha dzina la Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Iwo anachoka ku Bwalo Lalikulu akukondwa chifukwa anayesedwa oyenera kunyozedwa chifukwa cha dzina la Yesu. Onani mutuwo |