Machitidwe a Atumwi 4:11 - Buku Lopatulika11 Iye ndiye mwalawo woyesedwa wopanda pake ndi inu omanga nyumba, umene unayesedwa mutu wa pangodya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Iye ndiye mwalawo woyesedwa wopanda pake ndi inu omanga nyumba, umene unayesedwa mutu wa pangodya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Za Yesuyo mau a Mulungu akuti, “ ‘Mwala umene inu amisiri omanga nyumba mudaukana, womwewo wasanduka mwala wapangodya, wofunika koposa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye ndi “ ‘Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana, umenewo wasanduka mwala wa pa ngodya!’ Onani mutuwo |