Machitidwe a Atumwi 3:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anamgwira iye kudzanja lake lamanja, namnyamutsa; ndipo pomwepo mapazi ake ndi mfundo za kumapazi zinalimbikitsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anamgwira iye kudzanja lake lamanja, namnyamutsa; ndipo pomwepo mapazi ake ndi mfundo za kumapazi zinalimbikitsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Atatero adamgwira dzanja lamanja, namuimiritsa. Pompo mapazi ake ndi akakolo ake adalimba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo anamugwira dzanja lamanja, namuthandiza kuti ayimirire ndipo nthawi yomweyo mapazi ake ndi akakolo ake analimba. Onani mutuwo |