Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 3:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo iye anavomereza iwo, nalingirira kuti adzalandira kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo iye anavomereza iwo, nalingirira kuti adzalandira kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Iye nkuŵayang'anadi namaganiza kuti alandira kanthu kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Munthuyo anawayangʼanitsitsa kuyembekezera kuti alandira kanthu kuchokera kwa iwo.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 3:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo Petro, pompenyetsetsa iye pamodzi ndi Yohane, anati, Tiyang'ane ife.


Koma Petro anati, Siliva ndi golide ndilibe; koma chimene ndili nacho, ichi ndikupatsa, M'dzina la Yesu Khristu Mnazarayo, yenda.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa