Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 3:3 - Buku Lopatulika

3 ameneyo, pakuona Petro ndi Yohane akuti alowe mu Kachisi, anapempha alandire chaulere.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 ameneyo, pakuona Petro ndi Yohane akuti alowe m'Kachisi, anapempha alandire chaulere.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Pamene iye adaona Petro ndi Yohane akuloŵa m'Nyumba ya Mulungu, adaŵapempha kuti ampatseko kanthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Ataona Petro ndi Yohane ali pafupi kulowa anawapempha ndalama.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 3:3
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anatumiza Petro ndi Yohane, nati, Pitani mutikonzere ife Paska, kuti tidye.


Koma Petro ndi Yohane analikukwera kunka ku Kachisi pa ora lakupembedza, ndilo lachisanu ndi chinai.


Koma m'mene anagwira Petro ndi Yohane, anawathamangira pamodzi anthu onse kukhonde lotchedwa la Solomoni, alikudabwa ndithu.


Ndipo Petro, pompenyetsetsa iye pamodzi ndi Yohane, anati, Tiyang'ane ife.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa