Machitidwe a Atumwi 27:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo pamene tidapyola nyanja ya kunsi kwake kwa Silisiya ndi Pamfiliya, tinafika ku Mira wa Likiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo pamene tidapyola nyanja ya kunsi kwake kwa Silisiya ndi Pamfiliya, tinafika ku Mira wa Likiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tidawoloka nyanja mbali ya ku Silisiya ndi Pamfiliya nkumafika ku Mira, mzinda wa ku Likiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Titawoloka nyanja mbali ya gombe la Kilikiya ndi Pamfiliya, tinakafika ku Mura, mzinda wa ku Lukia. Onani mutuwo |