Machitidwe a Atumwi 27:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo pamene padatsimikizika kuti tipite m'ngalawa kunka ku Italiya, anapereka Paulo ndi andende ena kwa kenturiyo dzina lake Julio, wa gulu la Augusto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo pamene padatsimikizika kuti tipite m'ngalawa kunka ku Italiya, anapereka Paulo ndi andende ena kwa kenturiyo dzina lake Julio, wa gulu la Augusto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Zitatsimikizika kuti tiyenera kupita ku Italiya pa chombo, adampereka Paulo pamodzi ndi akaidi ena kwa mtsogoleri wa asilikali, dzina lake Julio, wa gulu la asilikali lochedwa gulu la Augusto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Zitatsimikizika kuti tiyenera kupita ku Italiya pa sitima ya pa madzi, anamupereka Paulo pamodzi ndi a mʼndende ena kwa msilikali wolamulira asilikali 100, dzina lake Yuliyo, amene anali wa gulu la asilikali lotchedwa, Gulu la Mfumu. Onani mutuwo |