Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 26:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo Agripa anati kwa Fesito, Tikadakhoza kumasula munthuyu, akadapanda kunena, Ndikatulukire kwa Kaisara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo Agripa anati kwa Fesito, Tikadakhoza kumasula munthuyu, akadapanda kunena, Ndikatulukire kwa Kaisara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Tsono Agripa adauza Fesito kuti, “Tikadammasula munthuyu akadapanda kupempha kuti mlandu wakewu ukazengedwe ndi Mfumu ya ku Roma.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Agripa anati kwa Festo, “Munthu uyu akanamasulidwa akanakhala kuti sanapemphe zokaonekera kwa Kaisara.”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 26:32
6 Mawu Ofanana  

Koma zitapita zaka ziwiri Porkio Fesito analowa m'malo a Felikisi; ndipo Felikisi pofuna kukonda Ayuda anamsiya Paulo m'nsinga.


Koma ndinapeza ine kuti sanachite kanthu koyenera imfa iye; ndipo popeza iye yekha anati akatulukire kwa Augusto, ndatsimikiza mtima kumtumizako.


ndiwo, atandifunsafunsa ine anafuna kundimasula, popeza panalibe chifukwa cha kundiphera.


Koma pakukanapo Ayuda, ndinafulumidwa mtima kutulukira kwa Kaisara; si kunena kuti ndinali nako kanthu kakunenera mtundu wanga.


Koma Ambuye anati kwa iye, Pita; pakuti iye ndiye chotengera changa chosankhika, chakunyamula dzina langa pamaso pa amitundu ndi mafumu ndi ana a Israele;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa