Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 24:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo Ayudanso anavomerezana naye, natsimikiza kuti izi zitero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Ayudanso anavomerezana naye, natsimikiza kuti izi zitero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ayudanso adavomereza, nanenetsa kuti zonsezo nzoona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ayuda anavomereza nanenetsa kuti zimenezi zinali zoona.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 24:9
13 Mawu Ofanana  

Amuna inu, ulemu wanga udzakhala wamanyazi kufikira liti? Mudzakonda zachabe, ndi kufunafuna bodza kufikira liti?


Inu muli ochokera mwa atate wanu mdierekezi, ndipo zolakalaka zake za atate wanu mufuna kuchita. Iyeyu anali wambanda kuyambira pachiyambi, ndipo sanaime m'choonadi, pakuti mwa iye mulibe choonadi. Pamene alankhula bodza, alankhula za mwini wake; pakuti ali wabodza, ndi atate wake wa bodza.


Ndipo kwa iye mudzakhoza kuzindikira pomfunsa nokha, za izi zonse timnenerazi.


natiletsa ife kuti tisalankhule ndi akunja kuti apulumutsidwe; kudzaza machimo ao nthawi zonse; koma mkwiyo wafika pa iwo kufikira chimaliziro.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa