Machitidwe a Atumwi 22:1 - Buku Lopatulika1 Amuna, abale, ndi atate, mverani chodzikanira changa tsopano, cha kwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Amuna, abale, ndi atate, mverani chodzikanira changa tsopano, cha kwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Inu abale anga ndi inu akuluakulu, mvereni ndiyankhe tsopano zimene akundinenezazi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Iye anati, “Inu abale anga ndi makolo anga, tamvani mawu akudziteteza kwanga.” Onani mutuwo |
Pakuti, taonani, ichi chomwe, chakuti mudamvetsedwa chisoni cha kwa Mulungu, khama lalikulu lanji chidalichita mwa inu, komanso chodzikonza, komanso mkwiyo, komanso mantha, komanso kukhumbitsa komanso changu, komanso kubwezera chilango! M'zonse munadzitsimikizira nokha kuti muli oyera mtima m'menemo.