Machitidwe a Atumwi 2:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo nanga ife timva bwanji, yense m'chilankhulidwe chathu chimene tinabadwa nacho? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo nanga ife timva bwanji, yense m'chilankhulidwe chathu chimene tinabadwa nacho? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nanga bwanji aliyense mwa ife akuŵamva akulankhula chilankhulo chakwao? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nanga bwanji aliyense wa ife akuwamva iwo mu chinenero cha kwawo? Onani mutuwo |