Machitidwe a Atumwi 2:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anadabwa onse, nazizwa, nanena, Taonani, awa onse alankhulawa sali Agalileya kodi? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anadabwa onse, nazizwa, nanena, Taonani, awa onse alankhulawa sali Agalileya kodi? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adadabwa, nathedwa nzeru ndipo adati, “Kodi onse akulankhulaŵa, si Agalileya? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Mothedwa nzeru anafunsana kuti, “Kodi anthu onse amene akuyankhulawa si Agalileya? Onani mutuwo |