Machitidwe a Atumwi 2:34 - Buku Lopatulika34 Pakuti Davide sanakwere Kumwamba ai; koma anena yekha, Ambuye anati kwa Mbuye wanga, khalani kudzanja lamanja langa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Pakuti Davide sanakwera Kumwamba ai; koma anena yekha, Ambuye anati kwa Mbuye wanga, khalani kudzanja lamanja langa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Pajatu Davide sadakwere kupita Kumwamba, koma iye yemwe adati, “ ‘Ambuye adauza Mbuye wanga kuti, Khala ku dzanja langa lamanja Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Pakuti si Davide anakwera kumwamba koma iye akuti, “ ‘Ambuye anawuza Ambuye anga kuti: Khala kudzanja langa lamanja Onani mutuwo |