Machitidwe a Atumwi 19:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo anati, Nanga mwabatizidwa m'chiyani? Ndipo anati, Mu ubatizo wa Yohane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anati, Nanga mwabatizidwa m'chiyani? Ndipo anati, Mu ubatizo wa Yohane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Paulo adaŵafunsa kuti, “Nanga tsono mudabatizidwa ndi ubatizo wotani?” Iwo adati, “Ndi ubatizo wa Yohane.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tsono Paulo anawafunsa kuti, “Nanga munabatizidwa ndi ubatizo wotani?” Iwo anati, “Ubatizo wa Yohane.” Onani mutuwo |