Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 17:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo pamene analandira chikole kwa Yasoni ndi enawo, anawamasula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo pamene analandira chikole kwa Yasoni ndi enawo, anawamasula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Koma Yasoni ndi anzake aja atalipira mlanduwo, akuluwo adaŵamasula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Iwo analipiritsa Yasoni ndi anzakewo ndipo anawamasula.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 17:9
2 Mawu Ofanana  

Koma Ayuda anadukidwa mtima, natenga anthu ena oipa achabe a pabwalo, nasonkhanitsa khamu la anthu, nachititsa phokoso m'mzinda; ndipo anagumukira kunyumba ya Yasoni, nafuna kuwatulutsira kwa anthu.


Ndipo anavuta anthu, ndi akulu a mzinda, pamene anamva zimenezi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa