Machitidwe a Atumwi 17:10 - Buku Lopatulika10 Pomwepo abale anatumiza Paulo ndi Silasi usiku kunka ku Berea; pamene iwo anafika komweko analowa m'sunagoge wa Ayuda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pomwepo abale anatumiza Paulo ndi Silasi usiku kunka ku Berea; pamene iwo anafika komweko analowa m'sunagoge wa Ayuda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Kutangoda, abale aja adapititsa Paulo ndi Silasi ku Berea. Atafika kumeneko, adakaloŵa m'nyumba yamapemphero ya Ayuda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mdima utagwa, abale anatumiza Paulo ndi Sila ku Bereya. Atafika kumeneko anapita ku sunagoge ya Ayuda. Onani mutuwo |