Machitidwe a Atumwi 16:2 - Buku Lopatulika2 Ameneyo anamchitira umboni wabwino abale a ku Listara ndi Ikonio. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ameneyo anamchitira umboni wabwino abale a ku Listara ndi Ikonio. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Abale a ku Listara ndi a ku Ikonio ankamtama Timoteoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Abale a ku Lusitra ndi Ikoniya anamuchitira iye umboni wabwino. Onani mutuwo |