Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 16:2 - Buku Lopatulika

2 Ameneyo anamchitira umboni wabwino abale a ku Listara ndi Ikonio.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ameneyo anamchitira umboni wabwino abale a ku Listara ndi Ikonio.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Abale a ku Listara ndi a ku Ikonio ankamtama Timoteoyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Abale a ku Lusitra ndi Ikoniya anamuchitira iye umboni wabwino.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 16:2
14 Mawu Ofanana  

Ndipo m'masiku awa anaimirira Petro pakati pa abale, nati (gulu la anthu losonkhana pamalo pomwe ndilo ngati zana limodzi ndi makumi awiri),


Koma iwo, m'mene adawasansira fumbi la ku mapazi ao anadza ku Ikonio.


Ndipo kunali pa Ikonio kuti analowa pamodzi m'sunagoge wa Ayuda, nalankhula kotero, kuti khamu lalikulu la Ayuda ndi Agriki anakhulupirira.


Pamene analalikira Uthenga Wabwino mumzindamo, nayesa ambiri ophunzira, anabwera ku Listara ndi Ikonio ndi Antiokeya,


iwo anamva, nathawira kumizinda ya Likaoniya, Listara ndi Deribe, ndi dziko lozungulirapo:


Ndipo anatuluka m'ndendemo, nalowa m'nyumba ya Lidia: ndipo pamene anaona abale, anawasangalatsa, namuka.


Chifukwa chake, abale, yang'anani mwa inu amuna asanu ndi awiri a mbiri yabwino, odzala ndi Mzimu ndi nzeru, amene tikawaike asunge ntchito iyi.


Koma muzindikira matsimikizidwe ake, kuti, monga mwana achitira atate wake, anatumikira pamodzi ndi ine Uthenga Wabwino.


Kuyeneranso kuti iwo akunja adzakhoza kumchitira umboni wabwino; kuti ungamgwere mtonzo, ndi msampha wa mdierekezi.


wa mbiri ya ntchito zabwino; ngati walera ana, ngati wachereza alendo, ngati adasambitsa mapazi a oyera mtima, ngati wathandiza osautsidwa, ngati anatsatadi ntchito zonse zabwino.


Momwemonso pali ntchito zokoma zinaonekera kale; ndipo zina zosati zotere sizingathe kubisika.


mazunzo, kumva zowawa; zotere zonga anandichitira mu Antiokeya, mu Ikonio, mu Listara, mazunzo otere onga ndawamva; ndipo m'zonsezi Ambuye anandilanditsa.


ndi kuti kuyambira ukhanda wako wadziwa malembo opatulika, okhoza kukupatsa nzeru kufikira chipulumutso, mwa chikhulupiriro cha mwa Khristu Yesu.


Pakuti momwemo akulu anachitidwa umboni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa