Machitidwe a Atumwi 16:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo anafikanso ku Deribe ndi Listara; ndipo taonani, panali wophunzira wina pamenepo, dzina lake Timoteo, amake ndiye Myuda wokhulupirira; koma atate wake ndiye Mgriki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo anafikanso ku Deribe ndi Listara; ndipo taonani, panali wophunzira wina pamenepo, dzina lake Timoteo, amake ndiye Myuda wokhulupirira; koma atate wake ndiye Mgriki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Paulo adafika ku Deribe ndi ku Listara. Kumeneko kunali wophunzira wina, dzina lake Timoteo. Mai wake anali Myuda wosanduka wokhulupirira, koma bambo wake anali Mgriki. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Paulo anafika ku Derbe ndi Lusitra, kumene kumakhala ophunzira wina dzina lake Timoteyo. Amayi ake anali Myuda wokhulupirira, koma abambo ake anali Mgriki. Onani mutuwo |