Machitidwe a Atumwi 14:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo khamu la mzindawo linagawikana; ena anali ndi Ayuda, koma ena anali ndi atumwi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo khamu la mudziwo linagawikana; ena anali ndi Ayuda, koma ena anali ndi atumwi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma anthu amumzindamo adagaŵikana, ena anali mbali ya Ayuda, ena anali mbali ya atumwi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Anthu a mu mzindamo anagawikana; ena anali mbali ya Ayuda, ena mbali ya atumwi. Onani mutuwo |