Machitidwe a Atumwi 14:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo pamene panakhala chigumukiro cha Agriki ndi cha Ayuda ndi akulu ao, cha kuwachitira chipongwe ndi kuwaponya miyala, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo pamene panakhala chigumukiro cha Agriki ndi cha Ayuda ndi akulu ao, cha kuwachitira chipongwe ndi kuwaponya miyala, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamenepo anthu akunja ndi Ayuda, pamodzi ndi akulu ao, adatsimikiza zoŵazunza ndi kuŵaponya miyala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pamenepo anthu a mitundu ina ndi Ayuda, pamodzi ndi atsogoleri awo anakonza chiwembu choti azunze atumwiwo ndi kuwagenda ndi miyala. Onani mutuwo |