Machitidwe a Atumwi 13:8 - Buku Lopatulika8 Koma Elimasi watsengayo (pakuti dzina lake litero posandulika) anawakaniza, nayesa kupatutsa kazembe asakhulupirire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma Elimasi watsengayo (pakuti dzina lake litero posandulika) anawakaniza, nayesa kupatutsa kazembe asakhulupirire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma kumeneko adapezanako ndi Elimasi, wamasenga uja (Elimasi ndiye kuti Wamasenga). Iyeyo adatengana nawo, kuwopa kuti bwanamkubwa uja angakhulupirire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Koma Elima wamatsengayo, (Elima tanthauzo lake ndi wamatsenga), anatsutsana nawo ndipo anafuna kumuletsa mkulu wa bomayo kuti asakhulupirire. Onani mutuwo |