Machitidwe a Atumwi 13:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo Paulo ananyamuka, nakodola ndi dzanja, nati, Amuna a Israele, ndi inu akuopa Mulungu, mverani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo Paulo ananyamuka, nakodola ndi dzanja, nati, Amuna a Israele, ndi inu akuopa Mulungu, mverani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Apo Paulo adaimirira nakweza dzanja kuti anthu akhale chete, ndipo adayamba kulankhula. Adati, “Inu Aisraele, ndi ena nonse oopa Mulungu, mverani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Atayimirira, Paulo anakweza dzanja lake ndi kuti, “Inu Aisraeli ndiponso inu a mitundu ina amene mumapembedza Mulungu, tandimverani! Onani mutuwo |