Machitidwe a Atumwi 13:12 - Buku Lopatulika12 Pamenepo kazembe, pakuona chochitikacho anakhulupirira, nadabwa nacho chiphunzitso cha Ambuye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamenepo kazembe, pakuona chochitikacho anakhulupirira, nadabwa nacho chiphunzitso cha Ambuye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pamene bwanamkubwa uja adaona zimene zidachitikazo, adakhulupirira. Adaadabwa nazo zimene iwo adaaphunzitsa za Ambuye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Pamene mkulu wa bomayo anaona zimene zinachitika anakhulupirira pakuti anadabwa ndi chiphunzitso cha Ambuye. Onani mutuwo |