Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 10:8 - Buku Lopatulika

8 ndipo m'mene adawafotokozera zonse, anawatuma ku Yopa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ndipo m'mene adawafotokozera zonse, anawatuma ku Yopa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Kornelio uja ataŵafotokozera zonse, adaŵatuma ku Yopa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iye anawafotokozera zonse zimene zinachitika ndipo anawatuma kuti apite ku Yopa.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 10:8
11 Mawu Ofanana  

Chilichonse dzanja lako lichipeza kuchichita, uchichite ndi mphamvu yako; pakuti mulibe ntchito ngakhale kulingirira ngakhale kudziwa, ngakhale nzeru, kumanda ulikupitako.


Ndipo pokayikakayika Petro mwa yekha ndi kuti masomphenya adawaona akuti chiyani, taonani, amuna aja otumidwa ndi Kornelio, atafunsira nyumba ya Simoni, anaima pachipata,


Pamenepo ndinatumiza kwa inu osachedwa; ndipo mwachita bwino mwadza kuno. Chifukwa chake taonani tilitonse pano pamaso pa Mulungu, kumva zonse Ambuye anakulamulirani.


Ndipo m'mene atachoka mngelo amene adalankhula naye, anaitana anyamata ake awiri, ndi msilikali wopembedza, wa iwo amene amtumikira kosaleka;


Potero, Mfumu Agripa, sindinakhale ine wosamvera masomphenya a Kumwamba;


Koma mu Yopa munali wophunzira dzina lake Tabita, ndilo kunena Dorika; mkazi ameneyo anadzala ndi ntchito zabwino ndi zachifundo zimene anazichita.


Ndipo popeza Lida ndi pafupi pa Yopa, m'mene anamva ophunzirawo kuti Petro anali pomwepo, anamtumizira anthu awiri, namdandaulira, Musachedwa mudze kwa ife.


Ndipo kudadziwika ku Yopa konse: ndipo ambiri anakhulupirira Ambuye.


Ndipo kunali, kuti anakhala iye mu Yopa masiku ambiri ndi munthu Simoni wofufuta zikopa.


kuti avumbulutse Mwana wake mwa ine, kuti ndimlalikire Iye mwa amitundu; pomwepo sindinafunsane ndi thupi ndi mwazi:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa