Machitidwe a Atumwi 10:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo tsopano tumiza amuna ku Yopa, aitane munthu Simoni, wotchedwanso Petro; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo tsopano tumiza amuna ku Yopa, aitane munthu Simoni, wotchedwanso Petro; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsopano tuma anthu ku Yopa kuti akaitane munthu wina, dzina lake Simoni, wotchedwanso Petro. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tsopano tuma anthu apite ku Yopa kuti akayitane munthu dzina lake Simoni Petro. Onani mutuwo |