Machitidwe a Atumwi 10:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo chinachitika katatu ichi; ndipo pomwepo chotengeracho chinatengedwa kunka kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo chinachitika katatu ichi; ndipo pomwepo chotengeracho chinatengedwa kunka kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Zimenezi zidachitika katatu, ndipo pompo chinthu chija chidatengedwa kupitanso kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Zimenezi zinachitika katatu ndipo nthawi yomweyo chinsalu chija chinatengedwanso kupita kumwamba. Onani mutuwo |