Machitidwe a Atumwi 10:11 - Buku Lopatulika11 ndipo anaona pathambo padatseguka, ndi chotengera chilinkutsika, chonga ngati chinsalu chachikulu, chogwiridwa pangodya zake zinai, ndi kutsikira padziko pansi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 ndipo anaona pathambo padatseguka, ndi chotengera chilinkutsika, chonga ngati chinsalu chachikulu, chogwiridwa pangodya zake zinai, ndi kutsikira padziko pansi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adaona kuthambo kutatsekuka, chinthu china chikutsikira pansi chooneka ngati chinsalu chachikulu chomangidwa pa nsonga zake zinai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anaona kuthambo kutatsekuka, ndi chinthu china chikutsitsidwa pansi chooneka ngati chinsalu chachikulu chomangidwa pa msonga zake zinayi. Onani mutuwo |