Machitidwe a Atumwi 10:10 - Buku Lopatulika10 koma m'mene analikumkonzera chakudya kudamgwera ngati kukomoka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 koma m'mene analikumkonzera chakudya kudamgwera ngati kukomoka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ali pamenepo, adamva njala, namafuna kudya. Koma pamene anthu ankakonza chakudya, iye adachita ngati wakomoka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Iye anamva njala ndipo anafuna chakudya, ndipo akukonza chakudyacho, iye anachita ngati wakomoka. Onani mutuwo |