Machitidwe a Atumwi 10:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo kunali munthu ku Kesareya, dzina lake Kornelio, kenturiyo wa gulu lotchedwa la Italiya, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo kunali munthu ku Kesareya, dzina lake Kornelio, kenturiyo wa gulu lotchedwa la Italiya, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ku Kesareya kunali munthu wina, dzina lake Kornelio. Iyeyu anali mkulu wa asilikali 100 achiroma, a m'gulu lotchedwa “Gulu la ku Italiya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ku Kaisareya kunali munthu wina dzina lake Korneliyo, mkulu wa asilikali 100 wa gulu la Italiya. Onani mutuwo |