Machitidwe a Atumwi 9:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo kunali, kuti anakhala iye mu Yopa masiku ambiri ndi munthu Simoni wofufuta zikopa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo kunali, kuti anakhala iye m'Yopa masiku ambiri ndi munthu Simoni wofufuta zikopa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Tsono Petro adakhala ku Yopa masiku ambiri kwa munthu wina, dzina lake Simoni, mmisiri wa zikopa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Petro anakhala ku Yopa kwa masiku ambiri kwa munthu wina, dzina lake Simoni, mmisiri wa zikopa. Onani mutuwo |