Machitidwe a Atumwi 1:7 - Buku Lopatulika7 Koma anati kwa iwo, Sikuli kwa inu kudziwa nthawi kapena nyengo, zimene Atate anaziika mu ulamuliro wake wa Iye yekha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma anati kwa iwo, Sikuli kwa inu kudziwa nthawi kapena nyengo, zimene Atate anaziika m'ulamuliro wake wa Iye yekha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Iye adati, “Si ntchito yanu kuti mudziŵe nthaŵi kapena nyengo pamene zidzachitike zimene Atate adakhazikitsa mwa mphamvu yao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yesu anawawuza kuti, “Sikofunika kuti mudziwe za nthawi kapena masiku amene Atate ayika mwa ulamuliro wawo. Onani mutuwo |