Luka 9:60 - Buku Lopatulika60 Koma anati kwa iye, Leka akufa aike akufa a eni okha; koma muka iwe nubukitse mbiri yake ya Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201460 Koma anati kwa iye, Leka akufa aike akufa a eni okha; koma muka iwe nubukitse mbiri yake ya Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa60 Yesu adamuuza kuti, “Aleke akufa aziika akufa anzao. Koma iwe, kalalike Ufumu wa Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero60 Yesu anati kwa iye, “Aleke akufa ayikane akufa okhaokha, koma iwe pita ukalalikire ufumu wa Mulungu.” Onani mutuwo |