Luka 9:57 - Buku Lopatulika57 Ndipo m'mene iwo analikuyenda m'njira, munthu anati kwa Iye, Ine ndidzakutsatani kumene kulikonse mukapitako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201457 Ndipo m'mene iwo analikuyenda m'njira, munthu anati kwa Iye, Ine ndidzakutsatani kumene kulikonse mukapitako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa57 Pamene iwo anali panjira, munthu wina adauza Yesu kuti, “Ndizikutsatani kulikonse kumene muzipita.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero57 Pamene iwo ankayenda mu msewu, munthu wina anati kwa Iye, “Inu ndikutsatirani kulikonse kumene mudzapita.” Onani mutuwo |