Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 9:56 - Buku Lopatulika

56 Ndipo anapita kumudzi kwina.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Ndipo anapita kumudzi kwina.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Pambuyo pake onse pamodzi adapita ku mudzi wina.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 ndipo iwo anapita ku mudzi wina.

Onani mutuwo Koperani




Luka 9:56
16 Mawu Ofanana  

Yang'anirani kuti musanyoze mmodzi wa ang'ono awa; pakuti ndinena kwa inu, kuti angelo ao apenya chipenyere nkhope ya Atate wanga wa Kumwamba.


monga Mwana wa Munthu sanadze kutumikiridwa koma kutumikira, ndi kupereka moyo wake dipo la anthu ambiri.


koma ndinena kwa inu, Musakanize munthu woipa; koma amene adzakupanda iwe pa tsaya lako lamanja, umtembenuzire linanso.


Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.


Koma Yesu anayankha nati, Lolani kufikira kumene. Ndipo anakhudza khutu lake, namchiritsa.


Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere.


Koma Iye anapotoloka nawadzudzula.


Ndipo m'mene iwo analikuyenda m'njira, munthu anati kwa Iye, Ine ndidzakutsatani kumene kulikonse mukapitako.


Siikudza mbala, koma kuti ikabe, ndi kupha, ndi kuononga. Ndadza Ine kuti akhale ndi moyo, ndi kukhala nao wochuluka.


Ndipo ngati wina akumva mau anga, ndi kusawasunga, Ine sindimweruza; pakuti sindinadze kudzaweruza dziko lapansi, koma kuti ndipulumutse dziko lapansi.


Pakuti Mulungu sanatume Mwana wake kudziko lapansi, kuti akaweruze dziko lapansi, koma kuti dziko lapansi likapulumutsidwe ndi Iye.


Musagonje kwa choipa, koma ndi chabwino gonjetsani choipa.


Mauwa ali okhulupirika ndi oyenera konse kuti awalandire, kuti Khristu Yesu anadza kudziko lapansi kupulumutsa ochimwa; wa iwowa ine ndine woposa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa