Luka 9:44 - Buku Lopatulika44 Alowe mau amenewa m'makutu anu; pakuti Mwana wa Munthu adzaperekedwa m'manja a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Alowe mau amenewa m'makutu anu; pakuti Mwana wa Munthu adzaperekedwa m'manja a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 “Mumvetse bwino zimene ndikuuzenizi: Mwana wa Munthu akudzaperekedwa kwa anthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 “Tamvetsetsani zimene ndikufuna kukuwuzani: Mwana wa Munthu akupita kukaperekedwa mʼmanja mwa anthu.” Onani mutuwo |