Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:56 - Buku Lopatulika

56 Ndipo atate wake ndi amake anadabwa; ndipo analamulira iwo asauze munthu aliyense chimene chinachitika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Ndipo atate wake ndi amake anadabwa; ndipo analamulira iwo asauze munthu aliyense chimene chinachitika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Makolo ake aja adazizwa kwambiri, koma Yesu adaŵalamula kuti asauze wina aliyense zimene zidaachitikazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 Makolo ake anadabwa, koma Iye anawalamulira kuti asawuze wina aliyense zimene zinachitikazo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:56
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu ananena naye, Ona, iwe, usauze munthu; koma muka, udzionetse wekha kwa wansembe, nupereke mtulo umene anaulamulira Mose, ukhale mboni kwa iwo.


Ndipo maso ao anaphenyuka. Ndipo Yesu anawauzitsa iwo, nanena, Yang'anirani, asadziwe munthu aliyense.


Ndipo Iye anamuuzitsa, kuti asanene kwa munthu aliyense; koma uchoke, nudzionetse wekha kwa wansembe, nupereke nsembe ya pa chikonzedwe chako, monga adalamulira Mose, kukhale umboni kwa iwo.


Ndipo mzimu wake unabwera, ndipo anauka pomwepo; ndipo Iye anawauza kuti ampatse kanthu ka kudya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa