Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:55 - Buku Lopatulika

55 Ndipo mzimu wake unabwera, ndipo anauka pomwepo; ndipo Iye anawauza kuti ampatse kanthu ka kudya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

55 Ndipo mzimu wake unabwera, ndipo anauka pomwepo; ndipo Iye anawauza kuti ampatse kanthu ka kudya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

55 Pomwepo moyo wake udabwereramo, iyeyo nkudzukadi nthaŵi yomweyo. Kenaka Yesu adaŵauza kuti ampatse chakudya mtsikanayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

55 Mzimu wake unabwerera, ndipo nthawi yomweyo anayimirira. Kenaka Yesu anawawuza kuti amupatse chakudya.

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:55
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anawalamulira kwambiri kuti asadziwe ichi munthu mmodzi, nawauza kuti ampatse iye kudya.


Ndipo Iye anamgwira dzanja lake, naitana, nati, Buthu, tauka.


Ndipo atate wake ndi amake anadabwa; ndipo analamulira iwo asauze munthu aliyense chimene chinachitika.


Ndipo womwalirayo anatuluka womangidwa miyendo ndi manja ndi nsalu za kumanda; ndi nkhope yake inazingidwa ndi mlezo. Yesu ananena nao, Mmasuleni iye, ndipo mlekeni amuke.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa