Luka 8:48 - Buku Lopatulika48 Ndipo Iye anati kwa iyeyu, Mwana wanga, chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe; muka ndi mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Ndipo Iye anati kwa iyeyu, Mwana wanga, chikhulupiriro chako chakupulumutsa iwe; muka ndi mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Apo Yesu adamuuza kuti, “Inu mwana wanga, chikhulupiriro chanu chakuchiritsani. Pitani ndi mtendere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Kenaka anati kwa iye, “Mwana wamkazi, chikhulupiriro chako chakuchiritsa. Pita mu mtendere.” Onani mutuwo |