Luka 8:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo zinampempha Iye, kuti asazilamulire zichoke kulowa ku chiphompho chakuya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo zinampempha Iye, kuti asazilamulire zichoke kulowa ku chiphompho chakuya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Kenaka mizimuyo idapempha Yesu kuti asailamule kuti ikaloŵe ku chiphompho chao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ndipo ziwandazo zimamupempha mobwerezabwereza kuti asazitumize ku dzenje la mdima. Onani mutuwo |
Chilombo chimene unachiona chinaliko, koma kulibe; ndipo chidzatuluka m'chiphompho chakuya, ndi kunka kuchitayiko. Ndipo adzazizwa iwo akukhala padziko amene dzina lao silinalembedwe m'buku la moyo chiyambire makhazikidwe a dziko lapansi, pakuona chilombo, kuti chinaliko, ndipo kulibe, ndipo chidzakhalako.