Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 8:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo anadza kwa Iye amake ndi abale ake, ndipo sanakhoze kumfika, chifukwa cha khamu la anthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo anadza kwa Iye amake ndi abale ake, ndipo sanakhoze kumfika, chifukwa cha khamu la anthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Amai ake ndi abale ake a Yesu adabwera kunyumbako, koma chifukwa cha kuchuluka kwa anthu, adaalephera kufika pamene panali Iyepo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Tsopano amayi ndi abale a Yesu anabwera kudzamuona Iye, koma analephera kuti afike pafupi ndi Iye chifukwa cha gulu la anthu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 8:19
4 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene abale ake anamva, anadza kudzamgwira Iye; pakuti anati adayaluka.


Ndipo anamuuza Iye, kuti, Amai wanu ndi abale anu alinkuima kunja, nafuna kuona Inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa