Luka 7:7 - Buku Lopatulika7 chifukwa chake ine sindinadziyesera ndekha woyenera kudza kwa Inu: koma nenani mau, ndipo mnyamata wanga adzachiritsidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 chifukwa chake ine sindinadziyesera ndekha woyenera kudza kwa Inu: koma nenani mau, ndipo mnyamata wanga adzachiritsidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nchifukwa chake sindidadziyesenso woyenera kudza kwa Inu. Koma mungonena mau okha kuti wantchito wanga achire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nʼchifukwa chake sindinadziyenereze ndi pangʼono pomwe kuti ndibwere kwa inu. Koma nenani mawu, ndipo wantchito wanga adzachira. Onani mutuwo |