Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 7:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo wakufayo anakhala tsonga, nayamba kulankhula. Ndipo anampereka kwa amake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo wakufayo anakhala tsonga, nayamba kulankhula. Ndipo anampereka kwa amake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Pamenepo wakufayo adakhala tsonga nayamba kulankhula, Yesu nkumupereka kwa mai wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Wakufayo anakhala tsonga ndi kuyamba kuyankhula, ndipo Yesu anamupereka mnyamatayo kwa amayi ake.

Onani mutuwo Koperani




Luka 7:15
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu, pakuika maliro a munthu wina, anaona gulu la nkhondo, naponya mtembo m'manda mwa Elisa; koma pamene mtembowo unakhudza mafupa a Elisa, wakufayo anauka, naima chilili.


Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.


Ndipo anayandikira, nakhudza chithatha; ndipo akumnyamulawo anaima. Ndipo Iye anati, Mnyamata iwe, ndinena ndi iwe, Tauka.


Ndipo mantha anagwira onsewo: ndipo analemekeza Mulungu, nanena kuti, Mneneri wamkulu wauka mwa ife; ndipo Mulungu wadzacheza ndi anthu ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa