Luka 7:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo kunali, katapita kamphindi, Iye anapita kumzinda, dzina lake Naini; ndipo ophunzira ake ndi mpingo waukulu wa anthu anapita naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo kunali, katapita kamphindi, Iye anapita kumudzi, dzina lake Naini; ndipo ophunzira ake ndi mpingo waukulu wa anthu anapita naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pambuyo pake Yesu adapita ku mudzi wina, dzina lake Naini. Ophunzira ake pamodzi ndi anthu ena ambirimbiri adatsagana naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Zitangotha izi, Yesu anapita ku mudzi wa Naini ndipo ophunzira ake ndi gulu lalikulu la anthu linapita naye pamodzi. Onani mutuwo |