Luka 6:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo kunali tsiku lina la Sabata, Iye analowa m'sunagoge, naphunzitsa. Ndipo munali munthu momwemo, ndipo dzanja lake lamanja linali lopuwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo kunali tsiku lina la Sabata, Iye analowa m'sunagoge, naphunzitsa. Ndipo munali munthu momwemo, ndipo dzanja lake lamanja linali lopuwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pa tsiku lina la Sabata Yesu adaloŵa m'nyumba yamapemphero nkumaphunzitsa. M'menemo munali munthu wina wopuwala dzanja lamanja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 La Sabata lina Iye analowa mʼsunagoge kukaphunzitsa ndipo mʼmenemo anapeza munthu wadzanja lolumala. Onani mutuwo |