Luka 6:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo Iye ananena kwa iwo, kuti, Mwana wa Munthu ali Mbuye wa tsiku la Sabata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo Iye ananena kwa iwo, kuti, Mwana wa Munthu ali Mbuye wa tsiku la Sabata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono Yesu popitiriza adaŵauza kuti, “Mwana wa Munthu ali ndi ulamuliro wonse pa zokhudza tsiku la Sabata.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kenaka Yesu anawawuza kuti, “Mwana wa Munthu ndi Ambuye wa Sabata.” Onani mutuwo |