Luka 6:47 - Buku Lopatulika47 Munthu aliyense wakudza kwa Ine, ndi kumva mau anga, ndi kuwachita, ndidzakusonyezani amene afanana naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Munthu aliyense wakudza kwa Ine, ndi kumva mau anga, ndi kuwachita, ndidzakusonyezani amene afanana naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 Munthu aliyense wodza kwa ine, namva mau anga nkumaŵagwiritsa ntchito, ndikuuzani amene amafanafana naye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Ine ndidzakuonetsani mmene alili munthu amene amabwera kwa Ine ndi kumva mawu anga ndi kuwachita. Onani mutuwo |